11/02/2022
ameretsa msipu ziudye ng'ombe ndi tsamba achite nazo munthu, atulutse chakudya chochokera mthaka ( plsm 104 v14) mulungu wathu ndi mulungu wa order anaika chilichonse mmalo mwache Ndikuti chigwire ntchito yake moyenera verse lo likuti ndizitsamba achitezo Munthu which means ifeyo kuti tipeze machilitso we need kugwilitsa ntchito chilengedwe muchingelezi zimemvekako bwino( herbs for the service fo man) zomwe zikuonetseratu kuti ifeyo tikiyenera kupanga depend on it, kuti tipeze relief kumatenda athu. Ndiye verse lo kumatepoko likuti anatulutse chakudya chochokera mthaka. Kodi pamene akufuna tiuzenji? Mene thupi lathuli linapangidwira ilikuyenera kulandira chakudya chomwe chili chofunika not kumangodya zili zonse ndizosadya zomwe ayi chakudya chochokera mthaka which mean zomera komaso zomwe zili organic not zothira mankhwala ndi fertilizer ayi ndichifukwa chake masiku ano tikudwala Matenda Monga bp diabetes, stroke Cancer kungochulapo yochepa chabe. Koma gwero la zonsezi ndi kudya ( eat) tisaiwale kuti munthu anachimwa chifukwa cha food ngati anthu tikufa ( death) nkhani yake ndi zakudya, ndiye pa death mukachotsapo D ali koyambilirayo ndikuchotsaponso H wakumapetoyo mupeza kuti nkhani ndi eat. Ndichomwe chikutipha anthufe. Hosea 4 v 6 mulungu akudalitseni mukhale ndi mmawa wopambana